Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 22:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma anapsa mtima Mulungu cifukwa ca kupita iye, ndipo mthenga wa Yehova anadziika m'njira wotsutsana naye, Ndipo anali wokwera pa buru wace, ndi anyamata ace awiri anali naye,

Werengani mutu wathunthu Numeri 22

Onani Numeri 22:22 nkhani