Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 21:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anthu anadza kwa Mose, nati, Tacimwa, popeza tinanena motsutsana ndi Yehova, ndi inu; pempherani kwa Yehova kuti aticotsere njokazi. Ndipo Mose anawapempherera anthu.

Werengani mutu wathunthu Numeri 21

Onani Numeri 21:7 nkhani