Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 21:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anthu ananena motsutsana ndi Mulungu, ndi Mose, ndi kuti, Mwatikwezeranji kuticotsa ku Aigupto kuti tifere m'cipululu? pakuti mkate ndi madzi palibe, ndi mtima wathu walema nao mkate wacabe uwu.

Werengani mutu wathunthu Numeri 21

Onani Numeri 21:5 nkhani