Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 20:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo Mose anatumiza amithenga ocokera ku Kadesi kumuka kwa mfumu ya Edomu, ndi kuti, Atero mbale wanu Israyeli, Mudziwa zowawa zonse zinatigwera;

Werengani mutu wathunthu Numeri 20

Onani Numeri 20:14 nkhani