Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 20:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, Popeza simunandikhulupirira Ine, kundipatula Ine pamaso pa ana a Israyeli, cifukwa cace simudzalowetsa msonkhano uwu m'dziko ndinawapatsali.

Werengani mutu wathunthu Numeri 20

Onani Numeri 20:12 nkhani