Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 19:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ali yense wakukhudza munthu wophedwa ndi lupanga, kapena mtembo, kapena pfupa la munthu, kapena manda, pathengo poyera, adzakhala wodetsedwa masiku asanu ndi awiri.

Werengani mutu wathunthu Numeri 19

Onani Numeri 19:16 nkhani