Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 18:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Unenenso ndi Alevi, nuti nao, Pamene mulandira kwa ana a Israyeli, limodzi la magawo khumi limene ndakupatsani likhale colowa canu cocokera kwao, muziperekako nsembe yokweza ya Yehova, limodzi la magawo khumi la limodzi la magawo khumi.

Werengani mutu wathunthu Numeri 18

Onani Numeri 18:26 nkhani