Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 16:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anasonkhana motsutsana pa Mose ndi Aroni, nanena nao, Mukula mphamvu inu, pakuti khamu lonse nlopatulika, onsewa, ndipo Yehova ali pakati pao; mudzikuza bwanji pa msonkhano wa Yehova?

Werengani mutu wathunthu Numeri 16

Onani Numeri 16:3 nkhani