Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 15:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo mukakonzera Yehova nsembe yamoto, nsembe yopsereza, kapena yophera, pocita cowinda ca padera, kapena nsembe yaufulu, kapena nsembe ya pa nyengo zanu zoikika, kumcitira Yehova pfungo lokoma, la ng'ombe kapena nkhosa;

Werengani mutu wathunthu Numeri 15

Onani Numeri 15:3 nkhani