Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 15:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kunena za khamu, pakhale lemba limodzi kwa inu, ndi kwa mlendo wakukhala kwanu, ndilo lemba losatha mwa mibadwo yanu; monga mukhala inu, momwemo mlendo pamaso pa Yehova.

Werengani mutu wathunthu Numeri 15

Onani Numeri 15:15 nkhani