Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 13:6-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Wa pfuko la Yuda, Kalebi mwana wa Yefune.

7. Wa pfuko la Isakara, Igali mwana wa Yosefe.

8. Wa pfuko la Efraimu, Hoseya mwana wa Nuni.

9. Wa pfuko la Benjamini, Paliti mwana wa Rafu.

10. Wa pfuko la Zebuloni, Gadiyeli mwana wa Sodi.

11. Wa pfuko la Yosefe, wa pfuko la Manase, Gadi mwana wa Susi.

12. Wa pfuko la Dani, Amiyeli mwana wa Gemali.

13. Wa pfuko la Aseri, Setri mwana wa Mikayeli.

Werengani mutu wathunthu Numeri 13