Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 13:29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Aamaleke akhala m'dziko la kumwera; ndi Ahiti, ndi Ayebusi, ndi Aamori, akhala ku mapiri, ndi Akanani akhala kunyanja, ndi m'mphepete mwa Yordano.

Werengani mutu wathunthu Numeri 13

Onani Numeri 13:29 nkhani