Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 11:33-35 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

33. Nyamayi ikali pakati pa mano, asanaitafune, Mulungu anapsa mtima pa anthuwa, ndipo Yehova anawakantha anthu ndi kukantha kwakukuru ndithu.

34. Ndipo anacha malowo dzina lace Kibiroti Hatava; popeza pamenepo anaika anthu osusuka.

35. Kucokera ku Kibiroti Hatava anthuwo anayenda kumka ku Hazeroti; nakhala ku Hazeroti.

Werengani mutu wathunthu Numeri 11