Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 1:8-19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

8. Wa Isakara, Netaneli mwana wa Zuwara.

9. Wa Zebuloni, Eliyabu mwana wa Heloni.

10. Wa ana a Yosefe: wa Efraimu, Elisama mwana wa Amihudi; wa Manase, Gamaliyeli mwana wa Pedazuri.

11. Wa Benjamini, Abidana mwana wa Gideoni.

12. Wa Dani, Ahiyezeri mwana wa Amisadai.

13. Wa Aseri, Pagiyeli mwana wa Okirani.

14. Wa Gadi, Eliyasafe mwana wa Deyueli.

15. Wa Nafitali, Ahira mwana wa Enani.

16. Iwo ndiwo oitanidwa a khamu, akalonga a mapfuko a makolo ao; ndiwo akuru a zikwizo za Israyeli.

17. Ndipo Mose ndi Aroni anatenga anthu awa, onenedwa maina ao;

18. nasonkhanitsa khamu lonse tsiku loyamba la mwezi waciwiri, ndipo iwo anawakumbira magwero ao kuchula mabanja ao, ndi nyumba za makolo ao, ndi kuwerenga maina kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu mmodzi mmodzi.

19. Monga Yehova anauza Mose, momwemo anawawerenga m'cipululu ca Sinai.

Werengani mutu wathunthu Numeri 1