Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 1:7-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

7. Wa Yuda, Nahesoni mwana wa Aminadabu.

8. Wa Isakara, Netaneli mwana wa Zuwara.

9. Wa Zebuloni, Eliyabu mwana wa Heloni.

10. Wa ana a Yosefe: wa Efraimu, Elisama mwana wa Amihudi; wa Manase, Gamaliyeli mwana wa Pedazuri.

11. Wa Benjamini, Abidana mwana wa Gideoni.

12. Wa Dani, Ahiyezeri mwana wa Amisadai.

13. Wa Aseri, Pagiyeli mwana wa Okirani.

14. Wa Gadi, Eliyasafe mwana wa Deyueli.

15. Wa Nafitali, Ahira mwana wa Enani.

16. Iwo ndiwo oitanidwa a khamu, akalonga a mapfuko a makolo ao; ndiwo akuru a zikwizo za Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Numeri 1