Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 7:56-63 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

56. ana a Neziya, ana a Hatifa.

57. Ana a akapolo a Solomo: ana a Sotai, ana a Sofereti, ana a Perida,

58. ana a Yaala, ana a Darikoni, ana a Gideli,

59. ana a Sefatiya, ana a Hatili, ana a Pokereti Hazebaimu, ana a Amoni.

60. Anetini onse, ndi ana a akapolo a Solomo, ndiwo mazana atatu mphambu makumi asanu ndi anai kudza awiri.

61. Ndipo okwera kucokera ku Telemela, Teleharisa, Kerubi, Adoni, ndi Imeri, ndi awa; koma sanakhoza kuchula nyumba za makolo ao, kapena mbumba zao, ngati ali a Israyeli;

62. ana a Delaya, ana a Tobiya, ana a Nekoda, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi anai kudza awiri.

63. Ndi a ansembe: ana a Hobaya, ana a Hokozi, ana a Barizilai, amene anadzitengera mkazi wa ana akazi a Barizilai Mgileadi, nachedwa ndi dzina lao.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 7