28. Amuna a ku Bete-Azimaveti, makumi anai kudza awiri.
29. Amuna a ku Kiriyati Yearimu, Kefiira, ndi Beeroti, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi anai kudza atatu.
30. Amuna a ku Rama ndi Geba, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza mmodzi.
31. Amuna a ku Mikimasi, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.
32. Amuna a ku Betele ndi Ai, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza atatu.
33. Amuna a ku Nebo winayo, makumi asanu kudza awiri.
34. Ana a Elamu winayo, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri ndi makumi asanu kudza anai.
35. Ana a Harimu, mazana atatu mphambu makumi awiri.