Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 7:25-32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

25. Ana a Gibeoni, makumi asanu ndi anai kudza asanu.

26. Amuna a ku Betelehemu ndi ku Netofa, zana limodzi mphambu makumi asanu ndi atatu kudza asanu ndi atatu.

27. Amuna a ku Anatoti, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

28. Amuna a ku Bete-Azimaveti, makumi anai kudza awiri.

29. Amuna a ku Kiriyati Yearimu, Kefiira, ndi Beeroti, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi anai kudza atatu.

30. Amuna a ku Rama ndi Geba, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza mmodzi.

31. Amuna a ku Mikimasi, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.

32. Amuna a ku Betele ndi Ai, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza atatu.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 7