Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 7:22-27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

22. Ana a Hasumu, mazana atatu mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

23. Ana a Bezai, mazana atatu mphambu makumi awiri kudza anai.

24. Ana a Harifi, zana limodzi mphambu khumi ndi awiri.

25. Ana a Gibeoni, makumi asanu ndi anai kudza asanu.

26. Amuna a ku Betelehemu ndi ku Netofa, zana limodzi mphambu makumi asanu ndi atatu kudza asanu ndi atatu.

27. Amuna a ku Anatoti, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 7