Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 7:20-26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

20. Ana a Adini, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu kudza asanu.

21. Ana a Aberi, a Hezekiya, makumi asanu ndi anai kudza asanu ndi atatu.

22. Ana a Hasumu, mazana atatu mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

23. Ana a Bezai, mazana atatu mphambu makumi awiri kudza anai.

24. Ana a Harifi, zana limodzi mphambu khumi ndi awiri.

25. Ana a Gibeoni, makumi asanu ndi anai kudza asanu.

26. Amuna a ku Betelehemu ndi ku Netofa, zana limodzi mphambu makumi asanu ndi atatu kudza asanu ndi atatu.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 7