Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 7:16-21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. Ana a Betai, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

17. Ana a Azigadi, zikwi ziwiri mphambu mazana atatu kudza makumi awiri ndi awiri.

18. Ana a Adonikamu, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi limodzi, kudza asanu ndi awiri.

19. Ana a Bigivai, zikwi ziwiri mphambu makumi asanu ndi limodzi kudza asanu ndi awiri.

20. Ana a Adini, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu kudza asanu.

21. Ana a Aberi, a Hezekiya, makumi asanu ndi anai kudza asanu ndi atatu.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 7