Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 6:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

m'menemo mudalembedwa, Kwamveka mwa amitundu, ndi Gasimu acinena, kuti iwe ndi Ayuda mulikulingirira za kupanduka; cifukwa cace mulikumanga lingali; ndipo iwe udzakhala mfumu yao monga mwa mau awa.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 6

Onani Nehemiya 6:6 nkhani