Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 6:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Kunali tsono, atamva Sanibalati, ndi Tobiya, ndi Gesemu M-arabu, ndi adani athu otsala, kuti ndidatha kumanga lingali, posatsalaponso popasuka; (ngakhale pajapo sindinaika zitseko pazipata);

2. anatumiza mau kwa ine Sanibalati ndi Gesemu, kuti, Tiyeni tikomane ku midzi ya ku cigwa ca Ono; koma analingirira za kundicitira coipa.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 6