Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 4:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace ndinawaika potera m'kati mwa linga, popenyeka; inde ndinaika anthu monga mwa mabanja ao, akhale nao malupanga ao, nthungo zao, ndi mauta ao.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 4

Onani Nehemiya 4:13 nkhani