Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 3:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi pa mbali pace Ezeri mwana wa Yesuwa, mkuru wa Mizipa, anakonza gawo lina, pandunji pokwerera ku nyumba yosungamo zida za nkhondo, popindirira linga.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 3

Onani Nehemiya 3:19 nkhani