Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 2:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma kunacitika mwezi wa Nisana, caka ca makumi awiri ca Aritasasta mfumu pokhala vinyo pamaso pace, ndinatenga vinyoyo ndi kuipatsa mfumu. Koma sindidakhala wacisoni pamaso pace ndi kale lonse.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 2

Onani Nehemiya 2:1 nkhani