Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 13:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Masiku awa ndinaona ku Yuda ena akuponda mphesa m'coponderamo dzuwa la Sabata, ndi akubwera nayo mitolo ya tirigu, ndi kuisenzetsa pa aburu; momwemonso vinyo, mphesa, ndi nkhuyu, ndi zosenza ziri zonse, zimene analowa nazo m'Yerusalemu dzuwa la Sabata, ndipo ndinawacitira umboni wakuwatsutsa tsikuti anagulitsa zakudya.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 13

Onani Nehemiya 13:15 nkhani