Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 12:9-21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. Ndi Bakibukiya ndi Uni, abale ao, anawayang'anira maulonda.

10. Ndi Yesuwa anabala Yoyakimu, ndi Yoyakimu anabala Eliasibi ndi Eliasibi anabala Yoyada,

11. ndi Yoyada anabala Yonatani, ndi Yonatani, anabala Yaduwa.

12. Ndi m'masiku a Yoyakimu ansembe akulu a nyumba za makolo ndiwo: wa Seraya, Meraya; wa Yeremiya, Hananiya;

13. wa Ezara, Mesulamu; wa Amariya, Yehohanana;

14. wa Maluki, Yonatani; wa Sebaniya, Yosefe;

15. wa Harimu, Adina; wa Merayoti, Helikai;

16. wa Ido, Zekariya; wa Ginetoni, Mesulamu;

17. wa Abiya, Zikiri; wa Minyamini, wa Moadiya, Pilitai;

18. wa Biliga, Samura; wa Semaya, Yehonatani;

19. ndi wa Yoyaribi, Matani; wa Yedaya, Uzi;

20. wa Salai, Kalai; wa Amoki, Eberi;

21. wa Hilikiya, Hasabiya; wa Yedaya, Netaneli.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 12