Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 12:5-15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. Miyamini, Maadiya, Biliga,

6. Semaya, ndi Yoyaribi, Yedaya,

7. Salu, Amoki, Hilikiya, Yedaya. Awa ndi akuru a ansembe ndi abale ao m'masiku a Yesuwa.

8. Ndi Alevi ndiwo Yesuwa, Binui, Kadimiyeli, Serebiya, Yuda, ndi Mataniya; iye ndi abale ace amatsogolera mayamiko.

9. Ndi Bakibukiya ndi Uni, abale ao, anawayang'anira maulonda.

10. Ndi Yesuwa anabala Yoyakimu, ndi Yoyakimu anabala Eliasibi ndi Eliasibi anabala Yoyada,

11. ndi Yoyada anabala Yonatani, ndi Yonatani, anabala Yaduwa.

12. Ndi m'masiku a Yoyakimu ansembe akulu a nyumba za makolo ndiwo: wa Seraya, Meraya; wa Yeremiya, Hananiya;

13. wa Ezara, Mesulamu; wa Amariya, Yehohanana;

14. wa Maluki, Yonatani; wa Sebaniya, Yosefe;

15. wa Harimu, Adina; wa Merayoti, Helikai;

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 12