Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 12:31-34 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

31. Pamenepo ndinakwera nao akuru a Yuda pa lingali, ndinaikanso oyamikira magulu awiri akuru oyenda molongosoka; lina loyenda ku dzanja lamanja palinga kumka ku cipata ca kudzala;

32. ndi pambuyo pao anayenda Hosaya, ndi limodzi la magawo awiri a akuru a Yuda,

33. ndi Azariya, Ezara ndi Mesulamu,

34. Yuda, ndi Benjamini, ndi Semaya, ndi Yeremiya,

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 12