Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 12:3-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Sekaniya, Rehumu, Meremoti,

4. Ido, Ginetoi, Abiya,

5. Miyamini, Maadiya, Biliga,

6. Semaya, ndi Yoyaribi, Yedaya,

7. Salu, Amoki, Hilikiya, Yedaya. Awa ndi akuru a ansembe ndi abale ao m'masiku a Yesuwa.

8. Ndi Alevi ndiwo Yesuwa, Binui, Kadimiyeli, Serebiya, Yuda, ndi Mataniya; iye ndi abale ace amatsogolera mayamiko.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 12