16. wa Ido, Zekariya; wa Ginetoni, Mesulamu;
17. wa Abiya, Zikiri; wa Minyamini, wa Moadiya, Pilitai;
18. wa Biliga, Samura; wa Semaya, Yehonatani;
19. ndi wa Yoyaribi, Matani; wa Yedaya, Uzi;
20. wa Salai, Kalai; wa Amoki, Eberi;
21. wa Hilikiya, Hasabiya; wa Yedaya, Netaneli.
22. M'masiku a Ehasibi, Yoyada, Yohanana, ndi Yoduwa, Alevi analembedwa akuru a nyumba za makolo; ansembe omwe, mpaka ufumu wa Dariyo wa ku Perisiya.