Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 12:12-19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

12. Ndi m'masiku a Yoyakimu ansembe akulu a nyumba za makolo ndiwo: wa Seraya, Meraya; wa Yeremiya, Hananiya;

13. wa Ezara, Mesulamu; wa Amariya, Yehohanana;

14. wa Maluki, Yonatani; wa Sebaniya, Yosefe;

15. wa Harimu, Adina; wa Merayoti, Helikai;

16. wa Ido, Zekariya; wa Ginetoni, Mesulamu;

17. wa Abiya, Zikiri; wa Minyamini, wa Moadiya, Pilitai;

18. wa Biliga, Samura; wa Semaya, Yehonatani;

19. ndi wa Yoyaribi, Matani; wa Yedaya, Uzi;

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 12