Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 12:11-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. ndi Yoyada anabala Yonatani, ndi Yonatani, anabala Yaduwa.

12. Ndi m'masiku a Yoyakimu ansembe akulu a nyumba za makolo ndiwo: wa Seraya, Meraya; wa Yeremiya, Hananiya;

13. wa Ezara, Mesulamu; wa Amariya, Yehohanana;

14. wa Maluki, Yonatani; wa Sebaniya, Yosefe;

15. wa Harimu, Adina; wa Merayoti, Helikai;

16. wa Ido, Zekariya; wa Ginetoni, Mesulamu;

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 12