Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 12:10-18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

10. Ndi Yesuwa anabala Yoyakimu, ndi Yoyakimu anabala Eliasibi ndi Eliasibi anabala Yoyada,

11. ndi Yoyada anabala Yonatani, ndi Yonatani, anabala Yaduwa.

12. Ndi m'masiku a Yoyakimu ansembe akulu a nyumba za makolo ndiwo: wa Seraya, Meraya; wa Yeremiya, Hananiya;

13. wa Ezara, Mesulamu; wa Amariya, Yehohanana;

14. wa Maluki, Yonatani; wa Sebaniya, Yosefe;

15. wa Harimu, Adina; wa Merayoti, Helikai;

16. wa Ido, Zekariya; wa Ginetoni, Mesulamu;

17. wa Abiya, Zikiri; wa Minyamini, wa Moadiya, Pilitai;

18. wa Biliga, Samura; wa Semaya, Yehonatani;

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 12