1. Ndipo ansembe ndi Alevi amene anakwera ndi Zerubabele mwana wa Sealtiyeli, ndi Yesuwa, ndi awa: Seraya, Yeremiya, Ezara,
2. Amariya, Maluki, Hatusi,
3. Sekaniya, Rehumu, Meremoti,
4. Ido, Ginetoi, Abiya,
5. Miyamini, Maadiya, Biliga,
6. Semaya, ndi Yoyaribi, Yedaya,
7. Salu, Amoki, Hilikiya, Yedaya. Awa ndi akuru a ansembe ndi abale ao m'masiku a Yesuwa.
8. Ndi Alevi ndiwo Yesuwa, Binui, Kadimiyeli, Serebiya, Yuda, ndi Mataniya; iye ndi abale ace amatsogolera mayamiko.
9. Ndi Bakibukiya ndi Uni, abale ao, anawayang'anira maulonda.