Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 12:1-10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo ansembe ndi Alevi amene anakwera ndi Zerubabele mwana wa Sealtiyeli, ndi Yesuwa, ndi awa: Seraya, Yeremiya, Ezara,

2. Amariya, Maluki, Hatusi,

3. Sekaniya, Rehumu, Meremoti,

4. Ido, Ginetoi, Abiya,

5. Miyamini, Maadiya, Biliga,

6. Semaya, ndi Yoyaribi, Yedaya,

7. Salu, Amoki, Hilikiya, Yedaya. Awa ndi akuru a ansembe ndi abale ao m'masiku a Yesuwa.

8. Ndi Alevi ndiwo Yesuwa, Binui, Kadimiyeli, Serebiya, Yuda, ndi Mataniya; iye ndi abale ace amatsogolera mayamiko.

9. Ndi Bakibukiya ndi Uni, abale ao, anawayang'anira maulonda.

10. Ndi Yesuwa anabala Yoyakimu, ndi Yoyakimu anabala Eliasibi ndi Eliasibi anabala Yoyada,

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 12