Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 11:28-32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

28. ndi m'Zikilaga, ndi m'Mekona ndi miraga yace,

29. ndi m'Enirimoni, ndi m'Zora, ndi m'Yarimuti,

30. Zanowa, Adulamu ndi midzi yao, Lakisi ndi minda yace, Azeka ndi miraga yace. Ndipo anamanga misasa kuyambira ku Beereseba mpaka cigwa ca Hinomu.

31. Ana a Benjamini omwe, kuyambira ku Geba pa Mikimasi, ndi Aiya, ndi pa Beteli ndi miraga yace,

32. pa Anatoti, Nobi, Ananiya,

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 11