Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 11:27-36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

27. ndi m'Hazarisuala, ndi m'Beereseba ndi miraga yace,

28. ndi m'Zikilaga, ndi m'Mekona ndi miraga yace,

29. ndi m'Enirimoni, ndi m'Zora, ndi m'Yarimuti,

30. Zanowa, Adulamu ndi midzi yao, Lakisi ndi minda yace, Azeka ndi miraga yace. Ndipo anamanga misasa kuyambira ku Beereseba mpaka cigwa ca Hinomu.

31. Ana a Benjamini omwe, kuyambira ku Geba pa Mikimasi, ndi Aiya, ndi pa Beteli ndi miraga yace,

32. pa Anatoti, Nobi, Ananiya,

33. Hazori, Rama, Gitaimu,

34. Hadidi, Zeboimu, Nebalati,

35. Lodi, ndi Ono, cigwa ca amisiri.

36. Ndi magawo a Levi anakhala ena ku Yuda, ndi ena ku Benjamini.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 11