Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 1:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

muchere khutu, ndi maso anu atseguke kumvera pemphero la kapolo wanu, ndilipempha pamaso panu tsopano apa msana ndi usiku, kupempherera ana a Israyeli akapolo anu, ndi kuulula zoipa za ana a Israyeli zimene tacimwira nazo Inu; inde tacimwa, ine ndi nyumba ya atate wanga.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 1

Onani Nehemiya 1:6 nkhani