Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nahumu 1:8-10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

8. Koma ndi cigumula cosefukira adzatha konse malo ace, nadzapitikitsira adani ace kumdima.

9. Mulingaliranji cotsutsana ndi Yehova? Iye adzatha psiti; nsautso siidzauka kawiri.

10. Pakuti cinkana akunga minga yoyangayanga, naledzera naco coledzeretsa cao, adzathedwa konse ngati ciputu couma.

Werengani mutu wathunthu Nahumu 1