Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mlaliki 5:7-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

7. Pakuti monga mu unyinji wa maloto muli zacabe motero mocuruka mau; koma dziopa Mulungu.

8. Ukaona anthu alikutsendereza aumphawi, ndi kucotsa cilungamo ndi ciweruzo mwaciwawa pa dera lina la dziko, usazizwepo; pakuti mkuru wopambana asamalira; ndipo alipo akuru ena oposa amenewo.

9. Phindutu la dziko lipindulira onse; ngakhale mfumu munda umthandiza.

Werengani mutu wathunthu Mlaliki 5