Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mlaliki 4:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pali mmodzi palibe waciwiri; inde, alibe mwana ngakhale mbale; koma nchito yace yonse iribe citsiriziro, ngakhale diso lace silikhuta cuma. Samati, Ndigwira nchito ndi kumana moyo wanga zabwino cifukwa ca yani? Icinso ndi cabe, inde, bvuto lalikuru.

Werengani mutu wathunthu Mlaliki 4

Onani Mlaliki 4:8 nkhani