Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mlaliki 2:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti pali munthu wina agwira nchito mwanzeru ndi modziwa nadzipinduliramo; koma adzapereka gawo lace kwa munthu amene sanagwirapo nchito. Icinso ndi cabe ndi coipa cacikuru.

Werengani mutu wathunthu Mlaliki 2

Onani Mlaliki 2:21 nkhani