Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mlaliki 2:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndani adziwa ngati adzakhala wanzeru pena citsiru? Koma adzalamulira nchito zanga zonse ndinasauka nazo, ndi kuzigwira mwanzeru kunja kuno. Icinso ndi cabe.

Werengani mutu wathunthu Mlaliki 2

Onani Mlaliki 2:19 nkhani