7. Pakuti m'kamwa mwanga mudzalankhula ntheradi,Zoipa zinyansa milomo yanga.
8. Mau onse a m'kamwa mwanga alungama;Mwa iwo mulibe zokhota ndi zopotoka.
9. Onsewo amveka ndi iye amene azindikira;Alungama kwa akupeza nzeru.
10. Landirani mwambo wanga, si siliva ai;Ndi nzeru kopambana ndi golidi wosankhika.
11. Pakuti nzeru iposa ngale,Ndi zonse tizifunitsa sizilingana nayo,