26. Asanalenge dziko, ndi thengo,Ngakhale ciyambi ca pfumbi la dziko.
27. Pamene anakhazika mlengalenga ndinali pompo;Pamene analemba pazozama kwete kwete;
28. Polimbitsa Iye thambo la kumwamba,Pokula akasupe a zozama.
29. Poikira nyanja malire ace,Kuti madzi asapitirire pa lamulo lace;Polemba maziko a dziko,
30. Ndinali pa mbali pace ngati mmisiri;Ndinamsekeretsa tsiku ndi tsiku,Ndi kukondwera pamaso pace nthawi zonse;