Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Miyambi 7:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Mwananga, sunga mau anga,Ukundike malangizo anga;

2. Sunga malangizo anga, nukhale ndi moyo;Ndi malamulo anga ngati mwana wa diso lako.

3. Uwamange pa zala zako,Uwalembe pamtima pako;

4. Nena kwa nzeru, Ndiwe mlongwanga;Nuche luntha mbale wako.

Werengani mutu wathunthu Miyambi 7