8. Siyanitsa njira yako kutari kwa iyeyo,Osayandikira ku khomo la nyumba yace;
9. Kuti ungapereke ulemu wako kwa ena,Ndi zaka zako kwa ankhanza;
10. Kuti mphamvu yako isakhutitse alendo,Ndi kuti usagwire nchito m'nyumba ya wacilendo;
11. Ungalire pa cimariziro cako,Pothera nyama yako ndi thupi lako;
12. Ndi kuti, Bwanji ndinada mwambo,Mtima wanga ndi kunyoza cidzudzulo;