Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Miyambi 4:7-11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

7. Nzeru ipambana, tatenga nzeru;M'kutenga kwako konseko utenge luntha.

8. Uilemekeze, ndipo idzakukweza;Idzakutengera ulemu pamene uifungatira.

9. Idzaika cisada ca cisomo pamtu pako;Idzakupatsa korona wokongola.

10. Tamvera mwananga, nulandire mau anga;Ndipo zaka za moyo wako zidzacuruka.

11. Ndakuphunzitsa m'njira ya nzeru,Ndakuyendetsa m'mayendedwe olungama.

Werengani mutu wathunthu Miyambi 4